MR TK

MR TK Contact information, map and directions, contact form, opening hours, services, ratings, photos, videos and announcements from MR TK, Lilongwe.

14/05/2024

😭😭😭😭

Admin please undibise osandivula chigobaπŸ™πŸ™
ndikufuna Anthu athandize kupemphela Ambuye andikhululukile pa zomwe ndinachita Malemu amuna anga, ndinalodza chifukwa choti ndinapeza ali ndi chibwezi chomwe amachipasa ndalama kwinaso amagulila zomvala zodula mkaziyo pomwe ine samandisamala.

nde ine nangoganiza zopeza mankhwala kuwalodza chifuna napsa mtima ndi zomwe amandichita. sinachite kufuna k*ti ndiwamphe koma zomwe amandipangazo ndizomwe zimandiwawa moyo mwanga ona ndinaganiza zoti ndingowampha😭😭😭. Nde panops saname ndikuvutika kwambili ana ndikukanika kuwasamala ndekha chifukwa shorp yomwe anandisiyila atamwalilayo inaduka zinthu sizimayenda chimwalilileni amuna angawo.

Ndinali maganizo achimwana simadziwa zomwe ndikuchita anali satana yemwe akandinamiza. chifukwa ine mawona ngati akamwalilamo sivutika chifukwa madalila shorp yoo k*ti ndiziyindesa kumapeza thandizo losamalila ana pakhomo.. koma tsoka lake shorp yoo inatha pano kuvutika kuchita kulakalaka amuna anga akanakhala moyo chifukwa simasowa kalikose pakhomo amathandiza, chabe sanje ndiyomwe inandipangisa k*ti ndifike powampha. kusaka maganyu anthu sakundilemba or mamuna oti ndipange naye chibwezi azithandiza akusowa or modzi ondifusila. please admin thandizeni ngati alipo angandipemphelele k*ti ambuye andikhululukile machimo anga ndipo andisungile chisisi ku akwawo amuna anga asadziwe zoti mwana wawo namumpha ndine chifukwa atha kundimpha. mamuna wanga anali munthu yekhayo yomwe kwawoko amadalila ndamene anali ochitikako bwino nde ataziwa zoti ndiwampha ine sangandisiye ndimoyo😭😭 please admin ngatiso pangapezeke mamuna ofuna mkazi ndipangeni naye connect ndipo asandiwone ineyo singazampheso mamuna panopa ndine munthu owopa Mulungu ndipo satana sangandigwilitse ntchito ndikuvutika ine saname 😭 please thandizeni osat kundiweludza ndikumafika paja pofuna kuzimangilila k*ti satile amuna anga koma ndikuwopa k*ti ana anga asowa owasamala. please help me ndasowa mtengo ogwila πŸ™

Follow nice page πŸ‘‰πŸ» MR TK

01/05/2024

Please admin post for me😭😭😭

nsaname munthune ndathodwa kwambiri nzimai wina p***a anandindiwuza za mankhwala a kondaine k*t ndadyetse amunanga coz ndinamudandaulira za mavuto anga a m'banja so ine k*tengeka ndinapangadi mpaka zinatheka kumudyetsa mamuna wanga

Now mamunayi akungoseka zilizonse, Ku ntchito wasiya kupita, moti kulikonse akumangondisata ndisaname wayamba kundinyasa. Nde ndinamuyimbira nzimai uja k*ti ngat pali mankhwala oti ndiziphidigule andiwuze coz zafika pa worse nde anandiyankha k*t zisamukhuze ndithana nazo ndekha😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭

Chonde abale ngat pali wina akudziwa k*ti zingathe bwanji zimenezi andiwuze coz mamuna wanga ndimakukonda kwambiri😭😭😭😭😭😭

Follow nice page πŸ‘‰πŸ» MR TK πŸ”₯MR TK

01/05/2024

Good morning guys
Am back
πŸ–πŸ–πŸ–

18/04/2024

```Timamenya amuna onse okana mimba mpaka kuvomera k*ti ndiyawo pa mtengo wabwino.
Tiimbireni phone mwansanga, ndipo simudzakhumudwa.
Anzanu akusimba lokoma kuno.

Timabwezeretsanso zibwenzi zok*tha mwadzidzidzi koma mwa Force.
Ndipo Chibwenzicho chikabwelera sichidzathanso.

Timamenyanso amuna onse ochedwa kumukwatira mkazi, asakuonongereni nthawi. Paja Nthawi ndi ndalama.

Timathanso kuyambitsa ndewu pa ukwati wa Ex wanu k*ti zilephereke, kaya k*tchalichi, kaya ku hall, mumasankha nokha. Ngati ndewu yalephereka timatha kugwera pa cake mwadala.

Timathanso kukhala boyfriend wodikilira, uku mukuyang'ana-yang'ana mwamuna wa serious.

Zonsezi timatha kupanga pa mtengo wabwino.```

18/04/2024

Hie tk kodi ma interview a mdf akuyamba monday wa ..lilongwe ndiliti kwaemwe akudxiwa tiuzeni pls..hide me koma

17/04/2024

Hello Mr tk

Abale Mr tk mamuna munandipanga connect last month kundithawa chongomuuza Kuti ndayima period sindikuyiwona ,

Mr tk chindipangileni connect week yoyamba tinadyana kwambiri,and panopa period sindinayiwone,so ndinagula ka pregnancy test ndipo kawonesa Kuti ndili ndi Mimba,ndamutumila Koma Pano wandipanga block am crying 😭 😭😭 Mr tk coz I believed him,Komaso ndili ndi Ana kale awiri omweso ndinachita kukanidwa so mpakana wachitatu Koma Mulungu wanga ndinalakwa chani ine😭😭😭😭.

Ndiye ndimati mwina ndimuyaluse chifukwa mwina akhozaso kubwera Kuti akufuna wina nkazi.kodi ndingalakwise kumuyika pa mbalambanda Kuti Anthu amuziwe so that asiye zomwe akupangazi.
Please ndithandizen maganizo.

Follow nice page πŸ‘‰πŸ» MR TK

16/04/2024

Mwagona guys
😬

15/04/2024

Hello Mr tk
Ndabwera Pano chifukwa cha ex boyfriend wanga Joseph mulenga from Blantyre ,

Mr tk ndikufuna Anthu andithandize kulilanga Galu πŸ• la mwamunayu limakonda kubwereka ma Galimoto πŸš™ kwama friends Ake nkumakanamiza Akazi mu Zomba Balaka Lilongwe and Mwanza Kuti ndiake,pamene Galu πŸ• limeneli lilibe kalikonse,likukhala ndi sister wake,

Mr tk Am a victim of Galu πŸ• ameneyu nditakumana nayo anandithira boza ine kumawona Ngati ndimamuna was dollar,kundipusisa mpaka k*tenga mimba chabe Kuti Mwanayo Anamwalira anabadwa ndi Vuto.

I know akuyenera kukhala pa page linoso chifukwa Kwa pemphero mphande sachota,

So please Mr tk post Kuti Akazi aziwe Kuti magalimoto amafika nawo Kwa akazi siake,gochita kubwereka.

Follow nice page πŸ‘‰πŸ» MR TK

14/04/2024

Hello Mr tk munthune ndili Ku South Africa komwe ndikugwira ntchito and pa nyumba ndinasiya nkazi wanga ndi Bambo anga omwe Ali munthu wachikulire,

Ndakhala ndik*tumiza ndalama every months Komaso ma groceries Kuti nkazi wanga ndi mwana wanga Komaso Bambo anga azidya,

Zonsezi ndimapanga nchifukwa choti bambo anga and nkazi wanga asamasoweke Koma Mr tk nkazi wanga wakhala ak*tenga ndalama zonse nkumapanga chitukuko kwawo,

Moti ndikunena Pano anamanga nyumba kwawo,pomwe bambo anga sakuwapasa zinthu zofunika zomwe amafuna pa moyo wawo as an old person,

Mr tk for over two years ine sindimaziwa Kuti bambo anga akusoweka zinthu zofunika yet ine mwezi uli onse ndimatuma ndalama,

Ex girlfriend wanga yomwe ndimayenda naye kale before I met nkazi wangayu came to see me kunyumba kwanthu and Bambo anga amamuziwa and atapita kukawona anapeza Kuti nkazi wanga anapita kwawo bambo anga alipo okha kusoweka ndi munthu oti nkuwaphikira chakudya, so ex wanga used her phone to call me and I spoke to my Dad,

Mr tk nthawi zambiri ndikayimba phone πŸ“± nkazi wanga amangoti bambo akugona so ndimakhala ndi ntima oti zonse zili bwino.

Mr tk Bambo anga alakhula zambiri zamomwe akukhalira,plus zoti nkazi wanga akumanga nyumba kwawo yomwe ine sindikuziwa kena Kali konse,

Mr tk Kodi pamenepa nditasiya nkazi wanga nk*tenga ex girlfriend wanga yomwe akuwoneka Kuti Ali ndi chikondi for my father ndingalakwise??? After all ex girlfriend wangayu sitinakambilanepo zoti chatha,chabe Kuti anachokapo nkupita Ku chitipa Kwa sister wake.

Please people ndithandizen maganizo,ineyo ndikufuna nkazi oti azindisamalira Bambo anga pomwe ndili kuno Ku South Africa

Follow nice page πŸ‘‰πŸ» MR TK

13/04/2024

Hello Mr tk Ndinagwiliridwa nda amuna achicoloured okwana 7 ana panopa ndili ndi Mimba Koma ma doctors ak*ti ndima twins,
Mr tk Ndinali mu nyumba ndi Mamuna wanga Kuno Ku Rodeepoort Newlands and ma coloured okwana 7 analowa mu room yanthu ndimipeni and ma screwdriver kufuna ndalama Koma Ife tinalibe ndalama mnyumba so anatilanda ma phone πŸ“±, kenako anampanga force mamuna wanga kumugoneka Pansi,then anayamba kundigwililira one by one,atamaliza anachoka nkupita😭😭😭,

Mr tk ndinakhala three weeks ndisakuva bwino, and Ku police yaku Sophia town tinΓ kapanga report in the morning Koma palibe yomwe anagwidwapo, after a month Mr tk Ndinayamba kupanga feel like am pregnant,so ndinapita pa clinic yina ndipo Anandiuza Kuti ndili ndi Mimba,

Kuyambira pamenepa ndakhala ndikuyambana ndi Mamuna wanga,iyeyo akufuna Mimba ikachisedwe Koma ineyo ndikukana kuwopa kufa, chifukwa iyeyo Amati akagule mankhwala ochosera Mimba mu Joberg Koma ineyo ndimakana chifukwa I don't trust them.

Zinthu zinafika povuta chifukwa Mamuna wanga anayamba kunena Kuti sangasunge Mimba ya zigawenga ,so I told him Kuti ndibwino ndipite Ku Malawi ndikachose Ku BLM osati kuno.koma amuna anga anati alibe ndalama zonditumizila Ku Malawi,so takhala tikusiyana Maganizo Kwa miyezi itatu, so last week ndinapita Ku chipatala kukakumana ndi doctor,and atandipanga check anapeza Kuti ndili ndi Mimba Yama twins,ana ndawiri mmimba mwanga,

Ndinauza amuna anga Zama report from the doctor Koma andiuza Kuti Ngati ndikufuna banja ndichotse mimba chifukwa iwowa sangakhale akusamala mimbayi.so I told him Kuti if he can give me ndalama ndikhoza kukachosa mimba Ku Malawi oasti kuno chifukwa ndikuwopa njira yomwe akunena amuna angawa.
please advise me,in as much as my husband akufuna ndichotse mimbayi mtima wanga ukuwopa,and panopa ak*ti andipasa ndalama end of this month Kuti ndipite Ku malawi ndikachose Koma at that time ndiye Kuti mimba izakhala for months and some weeks,
Kodi ndizotheka kuchosa or not???

Don't forget follow πŸ‘‰πŸ» MR TK

Address

Lilongwe

Telephone

+27687719155

Website

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when MR TK posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Contact The Business

Send a message to MR TK:

Share