Erifa Channel

Erifa Channel TOGETHER WE CAN...
(1)

In Him we believe In Him we see visionAmbuye ndipemphero langa kuti wina wake Chisomo chimugwere mu Week iyiii.  I pray ...
17/08/2026

In Him we believe
In Him we see vision

Ambuye ndipemphero langa kuti wina wake Chisomo chimugwere mu Week iyiii. I pray in the name of our lord Jesus chist
Amen πŸ‘‹πŸ‘‹πŸ‘‹πŸ‘‹πŸ‘‹πŸ‘‹
Landira chisomo
By
Apostle Eric

17/08/2026

Kukhala chete osalankhula umawononga zambiri.

17/08/2026

Bible limati
Ndife agonjesi

17/08/2026

Fuso from inbox

Apostle
Kodi munthu ungalemele ndi Salary?

Answer from Apostle
No.

Koma utha kuchita bwino ndi salary
Mwakuchita bwino utha kuzalemela.

Nanga inu mukuti bwanji?

17/08/2026

My Apostle
Miz Mzwakhe Tancredi

Ana a Mulungu wamoyo mvetsela nkhani iyii. God is love Ma Follow komaso ma  Ndimafuna ndidziwe Dela lomwe mukuchokela nd...
17/08/2026

Ana a Mulungu wamoyo mvetsela nkhani iyii.
God is love
Ma Follow komaso ma
Ndimafuna ndidziwe Dela lomwe mukuchokela nde tiwone komwe kuli ma followers ambiri a Erifa Channel
Chifukwa Apostle Eric, akulingalira chilinganizo ichi. Bible limati pali awiri pali atatu Mulungu amakhala pomwepo. Ndiye tizakumane awiri or atatu ( ) tizasonkhane mwa chikondi cha Mulungu.
Ndikuyamba kukambirana ziwiri zitatu, zokhuza Nkhani ya chikondi
Tiwone komwe kungapezeke awiri or atatu. Tizayambire kumeneko
Inu mukuwona bwanji?
Nenani Boma lomwe mukuchokela koma Dela.
Apostle Eric ali okonzeka kukuyendelani.

17/08/2026
17/08/2026

Anawalonjeza okhawo omusata iye osati akunja.

TIZIWELENGA BIBLE ANA A MULUNGU WAMOYO Munali munthu modzi inu mumafuna kumutumikira Mulungu ndi mtima wanu onse.Koma ch...
17/08/2026

TIZIWELENGA BIBLE ANA A MULUNGU WAMOYO

Munali munthu modzi inu mumafuna kumutumikira Mulungu ndi mtima wanu onse.
Koma chifukwa chakusawelenga Bible mwabwelela mbuyo.
Anthu akunamiza zambiri chifukwa chakusawelenga munavomeleza.
Ndikubwelela mbuyo. Njira zomwe akunamizani nazo.
1. Tonse ndife ochimwa
2. Palibe olungama (akapulumuke )
3. Azibusa akulemela ndi ndalama zanu
4. Chakhumi amadya ndi azibusa
5. Bible limazisusa lokha
6. Ubatizo wowona ndi uwuu
7. Tsiku lopemphera (Sabbath) ndi ili
8. Chomwe ukuchitachi ndi tchimo
9...
10...
Inu anakunamiza chan?................
Muziwelenga bible kuti uziziwa zowona za Mulungu
By
Apostle Eric

Ndipeleke morning choyamba Mwadzuka bwanji ana a Mulungu wamoyo
17/08/2026

Ndipeleke morning choyamba
Mwadzuka bwanji ana a Mulungu wamoyo

Address

Ntcheu

Opening Hours

Monday 07:00 - 17:00
Tuesday 07:00 - 17:00
Wednesday 07:00 - 17:00
Thursday 07:00 - 17:00
Friday 07:00 - 17:00
Saturday 07:00 - 19:00

Alerts

Be the first to know and let us send you an email when Erifa Channel posts news and promotions. Your email address will not be used for any other purpose, and you can unsubscribe at any time.

Shortcuts

Share